Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 149
  • “Mulungu Sakhoza Kunama”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mulungu Sakhoza Kunama”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi N’zosathekadi?
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Mverani Mulungu Kuti Mupindule ndi Malumbiro Ake
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 149

Nyimbo 149

“Mulungu Sakhoza Kunama”

(Ahebri 6:18)

1. M’lungu analonjeza Abrahamu,

Kuti adzadalitsa kwakukulu.

Abrahamu anakhulupilira;

Chifukwa M’lungu sakhoza kunama.

2. Kusonyeza kusasintha kwakeko,

Analoŵapo ndi lumbiro lake,

Tiyembekeza ndikumlemekeza,

Chifukwa M’lungu sakhoza kunama.

3. Kulimbitsa chikhulupiro chathu,

M’lungu ’natsimikiza mwalumbiro.

Tingagonjetse owukira onse;

Chifukwa M’lungu sakhoza kunama.

4. Yehova Wakumwamba ndiwowona,

Samasiyatu konse omgonjera.

Tidalira mawu, lumbiro lake

—Chifukwa M’lungu sakhoza kunama.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena