Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 90
  • Kulambira Yehova Ambuye Mfumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulambira Yehova Ambuye Mfumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Kuyenda m’Dzina la Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 90

Nyimbo 90

Kulambira Yehova Ambuye Mfumu

(Yesaya 2:3)

1. Yehova Ambuye Mfumu,

Mwabwezera chowonadi.

Kuŵala kwawonekadi,

Khamu likulambirani.

2. Chiwonjezekocho chadza

Kwa otumikira inu.

Alemekeza Mulungu

Nalambira inu nokha.

3. Sadzaphunziranso nkhondo,

Atsogoza utumiki;

Amalambira mwa mantha

Amvera lamulo lanu.

4. Tikondwa m’tsiku lanuli,

Pamene Ufumu wadza!

Mwana wanu alamula;

Tiimba mosangalala.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena