Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 38
  • Kusonyeza Kukhulupirika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kusonyeza Kukhulupirika
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kupambana Chiyeso cha Kukhulupirika
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Taonani Okhulupirika!
    Nsanja ya Olonda—1996
  • ‘Inu Nokha Ndinu Wokhulupirika’
    Yandikirani Yehova
  • Kukhulupirika—Pamtengo Wotani?
    Nsanja ya Olonda​—1990
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 38

Nyimbo 38

Kusonyeza Kukhulupirika

(Salmo 18:25)

1. Yehova ali ndi anthu

Olengeza dzinalo,

Monga mpingo wogonjera

Ndi wodziperekadi.

Pagomelo lauzimu

Amadya moyamika,

Amkondweretsa mumawu

Ndi zochita zawozo.

2. Tikhale odalirika

Mumpingo wa Mulungu,

Tisonyeze chipiliro

Chinkana pamavuto.

Tetezani zinthu zake,

Zisawonongedwetu;

Pamene zawopsezedwa,

Tidzachenjezeratu.

3. Tithandizedi abale,

Ofo’ka, atsopano,

Muntchito ndi m’kuphunzira

Tithandize mofatsa.

Monga m’moyo wabanjawo,

Tidzadaliranabe,

Tiyenera kukhalabe

Okhulupirikadi.

4. Kukhulupirika kwathu,

Tiyeni tisonyeze

Kwa oyenererawonso

Poyendatu m’Chikristu.

Kusonyezatu Satana

Ngwonama, Ya ngwowona.

Tikakhulupirikatu,

Tidzakondweretsa Ya.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena