Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 9
  • Madalitso a Yehova Alemeleretsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Madalitso a Yehova Alemeleretsa
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kuyembekeza pa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Ubwino Woyenda Mwangwiro
    Nsanja ya Olonda—2006
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 9

Nyimbo 9

Madalitso a Yehova Alemeleretsa

(Miyambo 10:22)

1. Yehova amatidalitsadi,

Pomwe timtumikira (mogwirizana).

Timakondwa kwambiri pobzala

Mawu opatsa nzeru.

2. Ngakhale mazunzo ngochuluka,

Ndipo timapilira (osalefuka),

Poti tiwona chifundo cha Ya,

Timalimbika mtima.

3. Ngati tichita zomwe tingathe,

Kuchita zabwinozo (moyenelera),

Yehova wokhulupirikayo,

Adzakondwera nafe.

4. Chotero tikhaletu achangu.

Tikhale ndi dalitso (mutidalitse)!

Adzavumbula chikondi chake;

Popandadi ululu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena