Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 203
  • Yehova Amatsogolera Anthu Ake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amatsogolera Anthu Ake
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndiye Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova
  • “Yehova Ndi M’busa Wanga”
    Imbirani Yehova
  • “Yehova ndi Mbusa Wanga”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 203

Nyimbo 203

Yehova Amatsogolera Anthu Ake

(Salmo 31:3)

1. M’lungu apereka chidziŵitso.

Alangiza anthu ake moleza mtima!

Watigaŵira kudzisankhira.

Amaika chowonadi m’mitima mwathu.

2. Munjira yake ndi nthaŵi yake,

Mwa mzimu woyera amavumbula zinthu.

“Kapolo” wake atidziŵitsa,

Mwachikondi mitima yathu ikondwera.

3. Chitsogozocho chiwongolera,

Chimapereka mphamvu kwa olungamawo.

Tikasinthadi m’kumvera kwathu,

Yehova adzatitsogoza m’dzina lake.

4. Tithokoza chithandizo chake,

Kuti tizindikire chowonadi chake.

Yehova ndi Bwenzi lathu ndithu;

Motsimikizira adzatitsogolera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena