Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 106
  • Tisamalire Mayendedwe Athu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tisamalire Mayendedwe Athu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Nthawi Ili Bwanji?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • “Dikirani” Chifukwa Nthawi ya Chiweruzo Yafika
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Chifukwa Chimene Mboni za Yehova Zimakhalira Zodikira
    Nsanja ya Olonda—1994
  • “Dikirani”!
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 106

Nyimbo 106

Tisamalire Mayendedwe Athu

(Aefeso 5:15)

1. Tisamalire Kuyenda kwathu,

Tikhale maso m’kuchenjera,

Tiombole nthaŵi poti

Satana alamula.

Tisamalire Malankhulidwe,

Tikhale maso ndi anzeru.

2. Tisamalire Kulalikira,

Tilimbikitsetu ofatsa.

Mwa kuphunziranso nawo,

Tidzawathandizadi.

Tisamalire Kaphunzitsidwe,

Tiwathandizetu ofatsa.

3. Tisamalire Kupatsa moni

Kwa opezeka mu’tumiki.

Monga Kristu Mbusa wathu,

Tisamalire “nkhosa.”

Tisamalire Kupatsa moni,

Ndi kusakhumudwitsa yense.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena