Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 16
  • Kondwererani Chiyembekezo Chaufumu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kondwererani Chiyembekezo Chaufumu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Yehova Poimba Nyimbo
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 16

Nyimbo 16

Kondwererani Chiyembekezo Chaufumu!

(Aroma 15:10-13)

1. Kondwani! Kondwani!

Kondwererani Ufumu!

Kondwani! Kondwani!

Ufumu wayamba!

Gwiritsani ufumuwo.

Khalani achangu.

Gwirani chiyembekezo.

Dziŵitsani onse.

Kondwani! Kondwani!

Dziwitsani Ufumuwo!

Kondwani! Kondwani!

Ufumu wayamba!

2. Kondwani! Kondwani!

Gwirani chiyembekezo!

Kondwani! Kondwani!

Dalirani M’lungu!

Yembekezerani zedi.

Musagwedezeke.

Simuyendanso mumdima;

Mwagudwa kuimfa.

Kondwani! Kondwani!

M’yembekezere Yehova!

Kondwani! Kondwani!

Peŵani Satana!

3. Imbani! Imbani!

Ufumu utilimbitsa!

Imbani! Imbani!

Tumikirani Ya!

Tukulani maso anu!

Ndinthaŵi yotuta,

Mumatulutsa zipatso,

Poyandika nkhosa.

Imbani! Imbani!

Mulungu alimbikitsa!

Imbani! Imbani!

Gwiritsa umphumphu!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena