Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 41
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalidwe la Ubwino
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuchirikiza Nyumba ya Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 41

Nyimbo 41

Lambirani Yehova Muli Achinyamata

Losindikizidwa

(Mlaliki 12:1)

1. Anyamata ndi atsikananu,

Ndinu ofunika kwa Mulungu.

Iye amakukondani zedi

Kudzeratu mwa makolo anu.

2. Lemekezani makolo anu,

Ndipo musapikisane nawo.

M’kakondedwa ndi anthu ndi M’lungu,

Mudzakondwera ndi unyamata.

3. Kumbukira Mlengi mu’nyamata

Uzikonda cho’nadi kwambiri.

Ukadzipereka kwa Yehova,

Iye ndithudi adzakondwera.

(Onaninso Sal. 71:17; Maliro 3:27; Aef. 6:1-3.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena