Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 87
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 87

Nyimbo 87

Tsopano Ndife Thupi Limodzi

Losindikizidwa

(Genesis 2:23, 24)

1. Fupa la mafupa anga,

Ndiwe mnofu wa mnofu wanga.

M’lungu wandipatsa mnzanga,

Inde wangawanga.

Tsopano tili amodzi,

Yehova ankafuna chonchi.

Monga mwamuna ndi mkazi,

Banja n’limeneli.

Mulungu atitsogolera.

Tsiku ndi tsiku

Chikondi tisonyeza.

Mmene talonjezerana

Zichitike, tizikondana.

Tilemekeze Yehova,

Ndipo ukhalebe wanga.

(Onaninso Gen. 29:18; Mlal. 4:9, 10; 1 Akor. 13:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena