Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 53
  • Tigwire Ntchito Mogwirizana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tigwire Ntchito Mogwirizana
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tizichita Zinthu Mogwirizana
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kugwirira Ntchito Pamodzi m’Chigwirizano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Banja la Yehova Lili ndi Umodzi Wamtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Mgwirizano wa Akhristu Umalemekeza Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 53

Nyimbo 53

Tigwire Ntchito Mogwirizana

Losindikizidwa

(Aefeso 4:3)

1. Tili m’gulu la Yehova,

Ndifedi osangalala,

Komanso ogwirizana,

N’zosangalatsadi.

Timasangalala

Ndi mgwirizano.

Zoti tichite n’zambiri,

Yesu atitsogolera.

Titumikire momvera,

Mogwirizananso.

2. Popempherera umodzi,

N’kukhala okoma mtima,

Chikondi chathu chikula,

Tidzasangalala.

Mtendere n’ngwabwino,

Utsitsimula.

Inde tikamakondana,

Tidzapezadi mtendere.

Tikhala ogwirizana,

Pomutumikira.

(Onaninso Mika 2:12; Zef. 3:9; 1 Akor. 1:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena