Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • cl tsamba 107
  • “Yehova Amakonda Chilungamo”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Yehova Amakonda Chilungamo”
  • Yandikirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Zinthu Zopanda Chilungamo Zidzatha Padzikoli?
    Nkhani Zina
  • “Njira Zake Zonse Ndi Zolungama”
    Yandikirani Yehova
  • Yehova—Gwero la Chilungamo Chenicheni
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Yandikirani Yehova
cl tsamba 107
Dzuwa likuwala kuchokera m’mitambo.

GAWO 2

“YEHOVA AMAKONDA CHILUNGAMO”

Masiku ano, padzikoli pakuchitika zinthu zopanda chilungamo zambiri ndipo anthu ambiri amanena kuti Mulungu ndi amene amachititsa zimenezi. Koma Baibulo limatiphunzitsa mfundo yolimbikitsa yakuti: “Yehova amakonda chilungamo.” (Salimo 37:28) M’chigawochi tiphunzira mmene iye wasonyezera kuti mawu amenewa ndi oona, zomwe zimapatsa anthu onse chiyembekezo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena