Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 62
  • Kodi Ndife Anthu a Ndani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ndife Anthu a Ndani?
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ndife A Ndani
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Ndife a Yani?
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 62

Nyimbo 62

Kodi Ndife Anthu a Ndani?

Losindikizidwa

(Aroma 14:8)

1. Iwe ndi wandani?

Umvera m’lungu uti?

Amene umam’gwadirayo,

Iye ndiye m’lungu wako.

Milungu iwiri

Sungaitumikire,

Sungalambire awiri onse,

Sungakhulupirike.

2. Iwe ndi wandani?

Umvera m’lungu uti?

Zilitu ndi iwe kusankha

Woona mwina wonama.

Kodi Kaisara

Udakamukondabe?

Kapena udzamvera Yehova

N’kuchita ntchito yake?

3. Ine ndi wandani?

Ndidzamvera Yehova.

Atate wanga wakumwamba

Ine ndidzam’sangalatsa.

Anandiwombola

Popatsa mwana wake,

Ndim’lambirabe, Ndi dzina lake

Ndililemekezabe.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 116:14, 18; 2 Tim. 2:19.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena