Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 76
  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Lolani “Mtendere wa Mulungu” Uchinjirize Mtima Wanu
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Mtendere​—Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • “Mtendere Ukhale Ndi Inu”
    Nsanja ya Olonda—1988
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 76

Nyimbo 76

Yehova Ndi Mulungu Wamtendere

Losindikizidwa

(Afilipi 4:9)

1. M’lungu wamtendere

M’tithandize tikhale

Ndi mtendere,

Makhalidwe abwino achuluke.

Malangizo anu,

Alowe mumtimamu.

Tikukupemphani

Mutipatse mtendere wanu.

2. Anthu m’dziko lonse

Akusowa mtendere.

Koma mtendere

Monga mvula muwazira ife.

Uchulukitseni

Ndipo tidalitseni.

Chifuniro chanu

Tikufuna tichidziwedi.

3. Mumatithandiza,

Mumatiunikira.

Mawu anu,

Mzimu wanu, zimatitsogolera.

Mtendere wangati

Mame ochulukadi.

Utitsitsimule,

Ukhazikitse mtima pansi.

(Onaninso Sal. 4:8; Afil. 4:6, 7; 1 Ates. 5:23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena