Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • th phunziro 9 tsamba 12
  • Kugwiritsa Ntchito Bwino Zinthu Zooneka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kugwiritsa Ntchito Bwino Zinthu Zooneka
  • Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
  • Nkhani Yofanana
  • Kugwiritsa Ntchito Mwaluso Zinthu Zooneka Pophunzitsa
    Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu
  • Muzigwiritsa Ntchito Mavidiyo Pophunzira ndi Anthu
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Kuthandiza Awo Amene Ali ndi AIDS
    Galamukani!—1994
  • Aids Zimene Makolo ndi Ana Ayenera Kudziŵa
    Galamukani!—1991
Onani Zambiri
Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
th phunziro 9 tsamba 12

PHUNZIRO 9

Kugwiritsa Ntchito Bwino Zinthu Zooneka

Lemba

Genesis 15:5

MFUNDO YAIKULU: Muzigwiritsa ntchito zinthu zooneka kuti anthu amvetse mfundo zikuluzikulu.

MMENE MUNGACHITIRE:

  • Muzisankha zinthu zimene zingathandizedi pophunzitsa. Mungagwiritse ntchito zithunzi, mapu, matchati kapena zinthu zina pofuna kutsindika mfundo zofunika osati timfundo ting’onoting’ono. Mukamaliza, anthu azikumbukira mfundo yaikuluyo osati zinthu zooneka zokhazo.

  • Zinthuzo zizikhala zoti aliyense atha kuziona.

    Mfundo yothandiza

    Muzikonzeratu zinthu zimene mukufuna kudzaonetsa anthu kukadali nthawi yambiri kuti mukambe nkhani.

MU UTUMIKI

Muzifunsa anthu kuti afotokoze zimene akuona pa zithunzi za m’mabuku athu. Muziwafunsa mafunso ena kuti mutsindike mfundo zofunika. Mukamaonetsa vidiyo, muziika chipangizo chanu m’njira yoti munthuyo aziona bwino. Si bwino kumalankhula uku vidiyo ili mkati.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena