Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 17
  • “Ndikufuna”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndikufuna”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndikufuna”
    Imbirani Yehova
  • Samalirani Ana ndi Akazi Amasiye M’mayesero Awo
    Nsanja ya Olonda—2001
  • “Ndifuna”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizitsanzira Chikondi cha Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 17

NYIMBO 17

“Ndikufuna”

Losindikizidwa

(Luka 5:13)

  1. 1. Khristu anatisonyeza

    Chikondi chachikuludi

    Pobwera padziko

    Kudzaphunzitsa

    M’mawu komanso m’zochita.

    Ankakonda anthu onse,

    Ankachiritsa odwala,

    Ankathandiza anthu mwakhama.

    Ananena: “Ndikufuna.”

  2. 2. Tikufuna kum’tsanzira

    M’zonse zomwe timachita.

    Timasonyezatu

    Kukoma mtima

    Tikalalikira anthu.

    Anzathu akavutika

    Tiwathandize mwamsanga

    Ndipo amasiye akapempha

    Tizinena: “Ndikufuna.”

(Onaninso Yoh. 18:37; Aef. 3:19; Afil. 2:7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena