Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 70
  • Fufuzani Anthu Oyenerera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Fufuzani Anthu Oyenerera
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Fufuzani Anthu Oyenerera
    Imbirani Yehova
  • Yehova Mulungu Wamkulu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Chilengedwe Chivumbula Ulemelero wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Sangalalani Ndi Ntchito Yotuta!
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 70

NYIMBO 70

Fufuzani Anthu Oyenerera

Losindikizidwa

(Mateyu 10:​11-​15)

  1. 1. Ambuye wathu anatisonyeza

    Njira yolalikirira.

    ‘Fufuzani anthu oyenerera

    Ofuna kumva choonadi.

    Muziwapatsa moni eni nyumba

    Ndi kuwafunira mtendere.

    Ngati sanakulandireni

    Sansani fumbi m’mapazi muchoke.’

  2. 2. Onse amene akulandirani

    Alandiranso Ambuye.

    Athandizeni kudziwa Yehova

    Ngati ali oyenerera.

    Musadere nkhawa zoti munene,

    Yehova akuthandizani.

    Mawu anu akakhala okoma,

    Ofatsa adzasangalala.

(Onaninso Mac. 13:48; 16:14; Akol. 4:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena