Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 40
  • Kodi Ndife A Ndani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ndife A Ndani
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ndife Anthu a Ndani?
    Imbirani Yehova
  • Kodi Ndife a Yani?
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kodi Ndinu ‘Okonzeka Kumvera’?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Adzakulimbitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 40

NYIMBO 40

Kodi Ndife A Ndani?

Losindikizidwa

(Aroma 14:8)

  1. 1. Iwe ndi wandani?

    Umvera m’lungu uti?

    Amene umamulambira

    Iye ndiye m’lungu wako.

    Milungu iwiri

    Sungaitumikire.

    Sungalambire iwiri yonse

    Sankhapo mmodzi yekha.

  2. 2. Iwe ndi wandani?

    Umvera m’lungu uti?

    Zili ndi iweyo kusankha

    Woona kaya wonama.

    Kodi Kaisara

    Udakamukondabe?

    Kapena udzamvera Yehova

    Ndikumutumikira?

  3. 3. Ine ndi wandani?

    Ndidzamvera Yehova.

    Ndikufuna kusangalatsa

    Atate wanga kumwamba.

    Anandigulatu.

    Ndidzamutumikira.

    Ndizimulambira iye yekha

    Ndi kumulemekeza.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 116:​14, 18; 2 Tim. 2:19.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena