Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 130
  • Muzikhululuka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzikhululuka
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikhululuka
    Imbirani Yehova
  • Khalani Wokhululukira
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Pitirizani Kukhululukirana Eni Okha’
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Khululukani Kuchokera Mumtima
    Nsanja ya Olonda—1999
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 130

NYIMBO 130

Muzikhululuka

Losindikizidwa

(Salimo 86:5)

  1. 1. Mwachikondi M’lungu

    Anapereka Yesu

    Kuti tikhululukidwe

    Ndi kudzathetsa imfa.

    M’lungu amakhululuka

    Ngati ife talapa.

    Nsembe ya dipo ya Yesu

    Imatithandizadi.

  2. 2. Tikamatsanzira

    Chifundo cha Yehova

    Pokhululukira anthu,

    Tidzakhululukidwa.

    Tikhale ololerana

    Ndipo tisamadane.

    Tizilemekeza onse

    Komanso kuwakonda.

  3. 3. Chifundo n’chabwino,

    Tonse tikhale nacho.

    Sitidzasunga zifukwa

    Tikakhumudwitsidwa.

    Tikatsanzira Yehova

    Yemwe ndi wachikondi,

    Tidzakhululukirana.

    Tidzafanana naye.

(Onaninso Mat. 6:12; Aef. 4:32; Akol. 3:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena