Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 121
  • Timafunika Kukhala Odziletsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Timafunika Kukhala Odziletsa
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tifunika Kukhala Odziletsa
    Imbirani Yehova
  • Kukulitsa Chipatso cha Kudziletsa
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Kudziletsa—Kodi Nchifukwa Ninji Kuli Kofunika Motero?
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Wonjezerani Kudziletsa pa Chizindikiritso Chanu
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 121

NYIMBO 121

Timafunika Kukhala Odziletsa

Losindikizidwa

(Aroma 7:​14-25)

  1. 1. Timakonda Yehova kwambiri

    Koma poti ndife anthu ochimwa,

    Timafunika kudziletsa.

    Mzimu umatithandizadi.

  2. 2. Tsiku ndi tsiku timayesedwa.

    Uchimowu ungatisocheretse

    Koma choonadi n’champhamvu.

    Yehova amatithandiza.

  3. 3. Tilemekeze dzina la M’lungu

    Muzochita ndiponso zolankhula.

    Cholinga chathu chiyenera

    Kukhala anthu odziletsa.

(Onaninso 1 Akor. 9:25; Agal. 5:23; 2 Pet. 1:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena