Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 36
  • Titeteze Mtima Wathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Titeteze Mtima Wathu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tetezani Mtima Wanu
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 36

NYIMBO 36

Titeteze Mitima Yathu

Losindikizidwa

(Miyambo 4:23)

  1. 1. Titeteze mtima wathu

    Tikhale ndi moyo.

    M’lungu amadziwa bwino

    Za mumtima mwathu.

    Mtima ndi wonyenga

    Ungamatisocheretse.

    Choncho tiganize bwino

    Timvere Yehova.

  2. 2. Timafunafuna M’lungu

    Tikamapemphera.

    Timathokozadi zonse

    Zomwe amachita.

    Zomwe amatiphunzitsa

    Timazitsatira

    Ndipo tikhulupirike,

    Timusangalatse.

  3. 3. Titeteze mtima wathu

    Tipewe zoipa.

    Mawu a Yehova M’lungu

    Atitsogolere.

    Anthu okhulupirika

    Amawakondadi.

    Choncho tizimulambira

    Monga bwenzi lathu.

(Onaninso Sal. 34:1; Afil. 4:8; 1 Pet. 3:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena