Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 59
  • Tamandani Ya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Ya
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tiyeni Tonse Titamande Ya
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Ya Limodzi Nane!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Mwana Wake Wodzozedwa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 59

NYIMBO 59

Tamandani Ya

Losindikizidwa

(Salimo 146:2)

  1. 1. Titamande

    Ya mokweza.

    Amatipatsa zonse zabwino.

    Tsiku lonse

    Tim’tamande.

    Ndi wachikondi ndi wamphamvunso

    Ndipo tilengeze dzina lake.

  2. 2. Titamande

    Ya chifukwa

    Amatimva tikamapemphera.

    Dzanja lake

    Ndi lamphamvu.

    Amalimbikitsa ofooka.

    Timalengeza za mphamvu zake.

  3. 3. Titamande

    Ya limodzi.

    Iye ndi Mulungu wolungama.

    Adzakonza Zolakwika

    Ndipo tonse

    tidzadalitsidwa.

    Timutamande mosangalala.

(Onaninso Sal. 94:​18, 19; 145:21; 147:1; 150:2; Mac. 17:25.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena