Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 157
  • Kudzakhala Mtendere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudzakhala Mtendere
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
    Imbirani Yehova
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 157

NYIMBO 157

Kudzakhala Mtendere

Losindikizidwa

(Salimo 29:11)

  1. 1. Pomwe dziko likusowa

    mtendere

    Ife tili ndi mtendere.

    Sitida nkhawa

    Chifukwa Yehova

    Adzathetsatu

    mavuto.

    (KOLASI)

    Padziko lapansi

    Padzakhalatu

    Mtendere wosatha.

    Mavuto akatha,

    Tidzapumula.

    Konse kudzakhala

    Mtendere.

  2. 2. Tikalowa m’dziko

    Latsopano

    Moyo udzasangalatsa.

    Mtendere womwe

    Tikulakalaka

    Yehova adzatipatsa.

    (KOLASI)

    Padziko lapansi

    Padzakhalatu

    Mtendere wosatha.

    Mavuto akatha,

    Tidzapumula.

    Konse kudzakhala

    Mtendere.

    (KOLASI)

    Padziko lapansi

    Padzakhalatu

    Mtendere wosatha.

    Mavuto akatha,

    Tidzapumula.

    Tidzasangalala!

    (KOLASI)

    Padziko lapansi

    Padzakhalatu

    Mtendere wosatha.

    Mavuto akatha,

    Tidzapumula.

    Konse kudzakhala

    Mtendere,

    Mtendere!

(Onaninso Sal. 72:1-7; Yes. 2:4; Aro. 16:20)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena