Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 77
  • Kuwala M’dziko Lamdima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuwala M’dziko Lamdima
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwala M’dziko Lamdima
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Kuunika Kumkabe Kuuŵala
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuunika kwa Mulungu Kumachotsa Mdima!
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Zinthu Zonse Zipangidwa Kukhala Zatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 77

NYIMBO 77

Kuwala M’dziko Lamdima

Losindikizidwa

(2 Akorinto 4:6)

  1. 1. M’dzikoli mulitu mdima.

    Anthu sakumvera.

    Kuwala kwatifikira

    Ngati m’bandakucha.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Wawala ngati dzuwa

    M’dziko lamdimali.

    Ukupatsa anthu

    Onse chiyembekezo.

    Mdima watha.

  2. 2. Tidzutse omwe agona

    Poti nthawi yatha.

    Komanso tiwathandize

    Tiwapempherere.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Wawala ngati dzuwa

    M’dziko lamdimali.

    Ukupatsa anthu

    Onse chiyembekezo.

    Mdima watha.

(Onaninso Yoh. 3:​19; 8:​12; Aroma 13:​11, 12; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena