Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 155
  • Chimwemwe Chosatha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chimwemwe Chosatha
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Chimwemwe Ndi Khalidwe Limene Mulungu Amapereka
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Tamandani Mfumu Yatsopano ya Dziko Lapansi
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Muzikonda Kwambiri Choonadi Panokha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 155

NYIMBO 155

Chimwemwe Chosatha

Losindikizidwa

(Salimo 16:11)

  1. 1. M’mwamba mwadzaza nyenyezi

    Zikuwalatu.

    Masananso Kukongola

    M’matikondadi.

    M’nalenga nyanja ndi mtunda

    Ndi zonse timaonazi,

    Munamva bwino.

    (KOLASI)

    Tonse tikusangalala

    N’za chipulumutso chathu

    Ndi dziko latsopano.

    Kukondedwa ndi ’nu M’lungu

    Ndi mwayidi wapadera.

    Ndinutu m’matipatsa

    Chimwemwe chosatha.

  2. 2. Tili n’zonse zofunika

    Zosangalatsa.

    Munatilenga mwaluso,

    Timamva bwino.

    Munatipatsatu mtima,

    Wofuna kukhala moyo

    Mpakatu kale.

    (KOLASI)

    Tonse tikusangalala,

    N’za chipulumutso chathu,

    Ndi dziko latsopano.

    Kukondedwa ndi ’nu M’lungu

    Ndi mwayidi wapadera.

    Ndinutu m’matipatsa

    Chimwemwe chosatha.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Popandatu Yesu

    Chimwemwe panalibe.

    Iyetu anatifera

    Ndiye chimwemwe n’chosatha.

    (KOLASI)

    Tonse tikusangalala,

    N’za chipulumutso chathu,

    Ndi dziko latsopano.

    Kukondedwa ndi ’nu M’lungu

    Ndi mwayidi wapadera.

    Ndinutu m’matipatsa

    Chimwemwe chosatha.

    (KOLASI)

    Tonse tikusangalala,

    N’za chipulumutso chathu,

    Ndi dziko latsopano.

    Kukondedwa ndi ’nu M’lungu

    Ndi mwayidi wapadera.

    Ndinutu m’matipatsa

    Chimwemwe chosatha.

(Onaninso Sal. 37:4; 1 Akor. 15:28.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena