Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 32
  • Khalani Kumbali ya Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Kumbali ya Yehova
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani ku Mbali ya Yehova
    Imbirani Yehova
  • Imani ndi Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Ndimasangalala Kuchita Zimene Mumafuna”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 32

NYIMBO 32

Khalani Kumbali ya Yehova

Losindikizidwa

(Ekisodo 32:26)

  1. 1. Kalekale tinali mumdima,

    Pokhala m’chipembedzo chabodza.

    Koma pano tikusangalala

    Tadziwa choonadi.

    (KOLASI)

    Khala kumbali ya Yehova M’lungu.

    Ukamamumvera, sangakusiye.

    Lengeza uthenga wamtenderewu.

    Ulamuliro wa M’lungu sudzatha.

  2. 2. Timakhala ku mbali ya M’lungu

    Polalikira kwa anthu onse

    Kuti nawo azisankha okha

    Kumvera M’lungu wathu.

    (KOLASI)

    Khala kumbali ya Yehova M’lungu.

    Ukamamumvera, sangakusiye.

    Lengeza uthenga wamtenderewu.

    Ulamuliro wa M’lungu sudzatha.

  3. 3. Sitidzamuopa Mdyerekezi.

    Tidzakhulupirira Yehova.

    Kaya adani angachuluke,

    M’lungu ndi mphamvu yathu.

    (KOLASI)

    Khala kumbali ya Yehova M’lungu.

    Ukamamumvera, sangakusiye.

    Lengeza uthenga wamtenderewu.

    Ulamuliro wa M’lungu sudzatha.

(Onaninso Sal. 94:14; Miy. 3:​5, 6; Aheb. 13:5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena