Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 61
  • Pitani Patsogolo Mboninu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitani Patsogolo Mboninu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Pitani Patsogolo Mboninu!
    Imbirani Yehova
  • Tiyeni, Mboninu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Pitirizani Kulalikira za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 61

NYIMBO 61

Pitani Patsogolo Mboninu

Losindikizidwa

(Luka 16:16)

  1. 1. Olimba m’nthawi yamapeto ino

    Ndi atumiki olengeza uthenga.

    Mdyerekezi amawatsutsa,

    Ndi mphamvu za Yehova samagonja.

    (KOLASI)

    Ndiye pitani patsogolo mboninu.

    Sangalalani pogwira ntchito yake.

    Uzani onse zadziko latsopano

    Mmene mudzakhale madalitso.

  2. 2. Tisatengeke ndi moyo wofewa.

    Tizipewa kusangalatsa dzikoli.

    Tikane zochita za dziko

    Ndi kukhala okhulupirikabe.

    (KOLASI)

    Ndiye pitani patsogolo mboninu.

    Sangalalani pogwira ntchito yake.

    Uzani onse zadziko latsopano

    Mmene mudzakhale madalitso.

  3. 3. Ufumu wa M’lungu ukunyozedwa,

    Dzina lake loyera likudetsedwa.

    Tiyeni tiziliyeretsa.

    Tililengeze kumitundu yonse.

    (KOLASI)

    Ndiye pitani patsogolo mboninu.

    Sangalalani pogwira ntchito yake.

    Uzani onse zadziko latsopano

    Mmene mudzakhale madalitso.

(Onaninso Eks. 9:​16; Afil. 1:7; 2 Tim. 2:​3, 4; Yak. 1:​27.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena