Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 6
  • Kumwamba Kumalengeza Ulemerero wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kumwamba Kumalengeza Ulemerero wa Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Miyamba Imalengeza Ulemelero wa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Zolengedwa Zimasonyeza Ulemerero wa Yehova
    Imbirani Yehova
  • Chilengedwe Chivumbula Ulemelero wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 6

NYIMBO 6

Kumwamba Kumalengeza Ulemerero wa Mulungu

Losindikizidwa

(Salimo 19)

  1. 1. Zakumwamba zimatamanda M’lungu.

    Zomwe analenga

    N’zochititsa chidwi.

    Zimalengeza ulemerero.

    Timazindikira kuti

    Alidi ndi mphamvu.

  2. 2. Malamulo a M’lungu ndi abwino.

    Mawu ake onse

    Amatiteteza.

    Amaweruzanso molungama.

    Mawu ake ndi oona,

    Amatithandiza.

  3. 3. Tiziopa Mulungu mpaka kale.

    Malamulo ake

    Ali ngati nyale

    Ndipotu amatitsogolera.

    Dzina lake loyeralo

    Tililemekeze.

(Onaninso Sal. 111:9; 145:5; Chiv. 4:11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena