Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 99
  • Abale Ambirimbiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Abale Ambirimbiri
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Khamu la Abale
    Imbirani Yehova
  • Unyinji wa Abale
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tsoka Lachiwiri Linali Makamu a Asilikali Okwera Pamahatchi
    Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
  • Zimene Muyenera Kudziwa Zokhudza Angelo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 99

NYIMBO 99

Abale Ambirimbiri

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 7:​9, 10)

  1. 1. Abale ambirimbiri.

    Inde ochuluka.

    Aliyense ndi mboni

    Yokhulupirika.

    Tilipodi ambiri.

    Tikuchulukabe.

    Tachokera m’mayiko onse

    Ndi mitundu yonse.

  2. 2. Abale ambirimbiri.

    Timalalikira

    Uthenga wabwinowu

    Kwa ofuna kumva.

    Pamene tafooka

    Yesu atipatsa

    Mpumulo ndi mphamvu zambiri.

    Sitimada nkhawa.

  3. 3. Abale ambirimbiri.

    Timatetezedwa

    Potumikira M’lungu

    Padziko lapansi.

    Tilipodi ambiri.

    Timalalikira.

    Timagwira ntchito ndi M’lungu

    Pomutumikira.

(Onaninso Yes. 52:7; Mat. 11:29; Chiv. 7:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena