Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 112
  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere
    Imbirani Yehova
  • Mtendere​—Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Mtendere Weniweni—Kodi Udzachokera Kuti?
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Lolani “Mtendere wa Mulungu” Uchinjirize Mtima Wanu
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 112

NYIMBO 112

Yehova Ndi Mulungu Wamtendere

Losindikizidwa

(Afilipi 4:9)

  1. 1. M’lungu wachikondi

    Mwalonjeza mtendere.

    Mutipatse mzimu wanu

    Uzitithandizabe.

    Chikhulupiriro

    Chimatithandizadi

    Kuti tikhale anzanu.

    Tilidi pamtendere.

  2. 2. Timamvetsa zinthu,

    Timaona kuwala.

    Mumatitsogolera

    M’dziko lomwe ndi lamdima.

    Nthawi idzafika

    Pomwe nkhondo zidzatha.

    Dalitsani khama lathu

    Tikhale amtendere.

  3. 3. Mulitu ndi gulu

    Kumwamba ndi padziko,

    Lomwe ndi logwirizana

    Lolengeza Ufumu.

    Mu Ufumu wanu

    Simudzakhala nkhondo.

    Tidzakhala mwamtendere

    Padziko mpaka kale.

(Onaninso Sal. 4:8; Afil. 4:​6, 7; 1 Ates. 5:​23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena