Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 34
  • Kuchita Zinthu Mokhulupirika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuchita Zinthu Mokhulupirika
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika
    Imbirani Yehova
  • Kuyenda Muumphumphu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yendani mu Umphumphu
    Nsanja ya Olonda—2004
  • N’chifukwa Chiyani Muyenera Kusunga Umphumphu?
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 34

NYIMBO 34

Kuchita Zinthu Mokhulupirika

Losindikizidwa

(Salimo 26)

  1. 1. Mulungu wanga mundiweruze,

    Muone ngati ndimakudalirani.

    Ndifufuzeni ndi kundiyesa.

    Konzani mtima wanga, mundidalitse.

    (KOLASI)

    Koma ine ndatsimikizadi

    Kumachita zinthu mokhulupirika.

  2. 2. Sindicheza ndi anthu oipa.

    Ndimadana ndi onyoza choonadi.

    Chonde musachotse moyo wanga

    Limodzi ndi anthu okonda zoipa.

    (KOLASI)

    Koma ine ndatsimikizadi

    Kumachita zinthu mokhulupirika.

  3. 3. Ndimakonda nyumba yanu M’lungu.

    Ndimasangalala kukulambirani.

    Ndidzayendadi kuguwa lanu

    Pokutamandani mokweza kwambiri.

    (KOLASI)

    Koma ine ndatsimikizadi

    Kumachita zinthu mokhulupirika.

(Onaninso Sal. 25:2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena