Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 90
  • Tizilimbikitsana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizilimbikitsana
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tizilimbikitsana
    Imbirani Yehova
  • “Pitirizani Kutonthozana ndi Kulimbikitsana”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Mungachite Kuti Mulungu Apitirize Kukukondani
    Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?
  • Fulumizanani ku Chikondano ndi Ntchito Zabwino—MotanI?
    Nsanja ya Olonda—1995
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 90

NYIMBO 90

Tizilimbikitsana

Losindikizidwa

(Aheberi 10:​24, 25)

  1. 1. Pomwe tikulimbikitsana

    Kutumikira Yehova,

    Chikondi chathu chimakula

    Ndipo timagwirizana.

    Chikondi cha anthu a M’lungu

    N’chothandiza kupirira.

    Timatetezedwa kwambiri

    Tikamakhala mumpingo.

  2. 2. Mawu a pa nthawi yabwino

    Amatilimbikitsadi.

    Mawu otilimbikitsawa

    Amachoka kwa abale.

    Kugwirira ntchito limodzi

    Kumatigwirizanitsa.

    Tizikhala olimbikitsa

    Ndipo tizithandizana.

  3. 3. Pamene tsiku la Yehova

    Layandikira kwambiri,

    Tipitirize kusonkhana

    Kuti tiyende ndi M’lungu.

    Tigwirizane ndi abale,

    Titumikire limodzi.

    Choncho tizilimbikitsana

    Kuti tikhulupirike.

(Onaninso Luka 22:32; Mac. 14:​21, 22; Agal. 6:2; 1 Ates. 5:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena