Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 79
  • Athandizeni Kukhala Olimba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Athandizeni Kukhala Olimba
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 79

NYIMBO 79

Athandizeni Kukhala Olimba

Losindikizidwa

(Mateyu 28:​19, 20)

  1. 1. Kuphunzitsa nkhosa za M’lungu

    Ndi mwayi wapadera.

    Yehova wawatsogolera

    Kukonda choonadi.

    (KOLASI)

    Yehova tikupemphatu

    Kuti muziwateteza.

    Mwa Yesu tikupemphera, athandizenibe

    Akhale olimba.

  2. 2. Mayesero akawagwera

    Tinkawapempherera.

    Tinkawaphunzitsa mwakhama,

    Pano adalitsidwa.

    (KOLASI)

    Yehova tikupemphatu

    Kuti muziwateteza.

    Mwa Yesu tikupemphera, athandizenibe

    Akhale olimba.

  3. 3. Akhale okudalirani

    Inu M’lungu ndi Yesu.

    Apirire pamayesero.

    Akalandire moyo.

    (KOLASI)

    Yehova tikupemphatu

    Kuti muziwateteza.

    Mwa Yesu tikupemphera, athandizenibe

    Akhale olimba.

(Onaninso Luka 6:​48; Mac. 5:​42; Afil. 4:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena