Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 106
  • Tikulitse Khalidwe la Chikondi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikulitse Khalidwe la Chikondi
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tizisonyeza Chikondi
    Imbirani Yehova
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
  • “Mulungu Ndi Chikondi”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 106

NYIMBO 106

Tikulitse Khalidwe la Chikondi

Losindikizidwa

(1 Akorinto 13:​1-8)

  1. 1. Chonde Mulungu mutipatse

    Makhalidwe anu onsewo.

    Koma lofunika kwambiri

    N’chikondi chomwe muli nacho.

    Ngati tilibe chikondichi

    Maluso athu ndi achabe.

    Tizisonyezana chikondi

    M’zochita ndi muzolankhula.

  2. 2. Chikondi ndi chokoma mtima

    Sichimafuna zake zokha.

    Sichimasunganso zifukwa,

    Chimakhululukira ena.

    Mavuto angakule bwanji

    Chikondi chimapirirabe.

    Chikondi sichimagonjanso.

    Chidzakhalapo mpaka kale.

(Onaninso Yoh. 21:17; 1 Akor. 13:13; Agal. 6:2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena