Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 84
  • Tizilalikira Modzipereka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizilalikira Modzipereka
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Timadzipereka
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 84

NYIMBO 84

Tizitumikira Modzipereka

Losindikizidwa

(Mateyu 9:​37, 38)

  1. 1. M’lungu wathu watipatsa

    Zomwe timafunikira

    Kuti tizisangalala

    Pomwe tikulalikira.

    (KOLASI)

    Tigwire ntchitoyi

    Modzipereka

    Ndipo kulikonse tipita

    Mofunitsitsa.

  2. 2. Padzikoli pali ntchito.

    Kosowa tidzapitako

    Tikatero tisonyeza

    Kuti timakonda anthu.

    (KOLASI)

    Tigwire ntchitoyi

    Modzipereka

    Ndipo kulikonse tipita

    Mofunitsitsa.

  3. 3. Kwathu kuno kuli ntchito.

    Tikuphunzira maluso.

    Taphunzira zinenero

    Ndipo tikulalikira.

    (KOLASI)

    Tigwire ntchitoyi

    Modzipereka

    Ndipo kulikonse tipita

    Mofunitsitsa.

(Onaninso Yoh. 4:​35; Mac. 2:8; Aroma 10:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena