Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 129
  • Tipitirizebe Kupirira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tipitirizebe Kupirira
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tipirirabe Mpaka Mapeto
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Muzitsanzira Yehova pa Nkhani ya Kupirira
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chipiriro—Nchofunika kwa Akristu
    Nsanja ya Olonda—1993
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 129

NYIMBO 129

Tipitirizebe Kupirira

Losindikizidwa

(Mateyu 24:13)

  1. 1. Tizipirira

    Mayesero ngati Yesu.

    Anavutika

    Koma ankasangalala

    Ndi chiyembekezo.

    Analimba mtima.

    (KOLASI)

    Tikhale opirira.

    Tizilalikira.

    M’lungu amatikonda

    Adzatithandiza kupirira.

  2. 2. Tingakumane

    Ndi mavuto ochuluka,

    Tidikirebe

    Moyo wosatha m’tsogolo.

    Tikulakalaka

    Mtendere wosatha.

    (KOLASI)

    Tikhale opirira.

    Tizilalikira.

    M’lungu amatikonda

    Adzatithandiza kupirira.

  3. 3. Sitimaopa

    Kapena kukayikira.

    Titumikire

    Mpaka tsiku lomaliza.

    Tsiku la Yehova

    Lilidi pafupi.

    (KOLASI)

    Tikhale opirira.

    Tizilalikira.

    M’lungu amatikonda

    Adzatithandiza kupirira.

(Onaninso Mac. 20:​19, 20; Yak. 1:​12; 1 Pet. 4:​12-​14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena