Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 48
  • Tiziyenda ndi Yehova Tsiku Lililonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiziyenda ndi Yehova Tsiku Lililonse
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Timayenda ndi Yehova Tsiku Lililonse!
    Imbirani Yehova
  • Kuyenda ndi Yehova Masiku Onse
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Muziyenda Ndi Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Muyenda ndi Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 48

NYIMBO 48

Tiziyenda Ndi Yehova Tsiku Lililonse

Losindikizidwa

(Mika 6:8)

  1. 1. Timayenda ndi Yehova

    Nthawi zonse modzichepetsa.

    Amatikomera mtima

    Tikamamusangalatsadi.

    Mwa nsembe ya Yesu Khristu,

    Tingayende ndi M’lungu.

    Choncho timadzipereka

    Potumikira Yehova.

  2. 2. Mapeto ali pafupi

    Ndipo Satana ndi wokwiya.

    Timatsutsidwa kwambiri

    Choncho tingamachite mantha.

    Yehova atiteteza

    Ngati timamumvera.

    Tizimutumikirabe

    Ndi kum’konda nthawi zonse.

  3. 3. M’lungu amatithandiza

    Ndi mzimu ndi mawu akenso.

    Iye amatithandiza

    Kudzeranso mu mpingo wake.

    Tikayenda ndi Yehova

    Tidzachita zabwino.

    Choncho tikhulupirike

    N’kukhala odzichepetsa.

(Onaninso Gen. 5:24; 6:9; 1 Maf. 2:​3, 4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena