Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 150
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 150

NYIMBO 150

Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke

Losindikizidwa

(Zefaniya 2:3)

  1. 1. Mitundu ya anthu

    Ikutsutsabe Yesu.

    Ulamuliro wa anthu

    Utha watero M’lungu.

    Ufumu wa M’lungu

    Ukulamuliradi.

    Yesu adzachotsa adani.

    Adzatha posachedwa.

    (KOLASI)

    Bweranitu kwa Yehova

    Kuti mudzapulumuke.

    Musakayike,

    Muzimumvera,

    Mukhale kumbali yake.

    Adzakupulumutsani

    Ndi mphamvu zake.

  2. 2. Anthu akusankha

    Kumvetsera uthenga.

    Timalalikira onse.

    Enatu amakana.

    Tikamavutika

    Tisakhale ndi mantha.

    M’lungu adzatisamalira

    Timukhulupirire.

    (KOLASI)

    Bweranitu kwa Yehova

    Kuti mudzapulumuke.

    Musakayike,

    Muzimumvera,

    Mukhale kumbali yake.

    Adzakupulumutsani

    Ndi mphamvu zake.

(Onaninso 1 Sam. 2:9; Sal. 2:​2, 3, 9; Miy. 2:8; Mat. 6:33.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena