Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 104
  • Mzimu Woyera Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mzimu Woyera Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Mphatso Yochokera kwa Mulungu ya Mzimu Woyera
    Imbirani Yehova
  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kutsogoleredwa ndi Mzimu wa Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Mphatso ya Yehova ya Mzimu Woyera
    Nsanja ya Olonda—1992
  • Mzimu Woyera Ndi Mphamvu Yofunika Pamoyo Wanu
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 104

NYIMBO 104

Mzimu Woyera Ndi Mphatso Yochokera Kwa Mulungu

Losindikizidwa

(Luka 11:13)

  1. 1. Yehova M’lungu ndinu wamkulu.

    Mumaposa mitima yathu.

    Muzitithandiza pamavuto.

    Mutilimbitse ndi mzimu wanu.

  2. 2. Ndife ochimwa, operewera.

    Nthawi zina timalakwitsa.

    Tikupempha mutipatse mzimu

    Utitsogolere nthawi zonse.

  3. 3. Tikafooka ndi kukhumudwa,

    Mzimu uzitilimbikitsa.

    Mutipatse mphamvu tisagonje.

    Muzitipatsa mzimu woyera.

(Onaninso Sal. 51:11; Yoh. 14:26; Mac. 9:31.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena