Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • nwt tsamba 2244
  • B15 Kalendala ya Chiheberi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • B15 Kalendala ya Chiheberi
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mukudziwa?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Mudzaphunzira Kuchokera Kunyengo?
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Kalendala ya Zaulimi ya mu “Dziko Lokoma”
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Madyerero Osaiŵalika a m’Mbiri ya Israyeli
    Nsanja ya Olonda—1998
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
B15 Kalendala ya Chiheberi

B15

Kalendala ya Chiheberi KUSIYANASIYANA KWA NYENGO

Losindikizidwa

NISANI (ABIBU) March—April

14 Pasika

15-21 Mkate Wopanda Zofufumitsa

16 Nsembe ya zipatso zoyamba kucha

Yorodano ankasefukira chifukwa cha mvula ndi madzi osungunuka

Balere

IYARA (ZIVI) April—May

14 Pasika Wochitika Nthawi Yake Itadutsa

Nthawi ya chilimwe, kumwamba kopanda mitambo

Tirigu

SIVANI May—June

6 Chikondwerero cha Masabata (Pentekosite)

Kunja kunkatentha koma kunkakhala mpweya wabwino

Tirigu, nkhuyu zoyambirira

TAMUZI June—July

 

Kutentha kunkawonjezereka, mame ankagwa ambiri

Mphesa zoyambirira

ABI July—August

 

Kutentha kunkafika pachimake

Zipatso zamʼchilimwe

ELULI August—September

 

Kutentha kunkapitirira

Kanjedza, mphesa ndi nkhuyu

TISHIRI (ETANIMU) September—October

1 Tsiku loliza lipenga

10 Mwambo Wophimba Machimo

15-21 Chikondwerero cha Misasa

22 Msonkhano wapadera

Chilimwe chikutha, mvula ikuyamba

Kulima

HESHIVANI (BULI) October—November

 

Mvula yowaza—

Maolivi

KISILEVI November—December

25 Chikondwerero cha Kupereka Kachisi wa Mulungu

Mvula inkawonjezereka, madzi ankaundana mʼmapiri

Nyengo yozizira ziweto zinkakhala mʼkhola

TEBETI December—January

 

Kunkazizira kwambiri, kunkagwa mvula, madzi ankaundana mʼmapiri

Zomera zikukula

SEBATI January—February

 

Kuzizira kunkacheperako, mvula inkapitiriza kugwa

Amondi ankachita maluwa

ADARA February—March

14, 15 Purimu

Kunkachitika mabingu, kunkagwa mvula yamatalala

Fulakesi

VEADARA March

Pa zaka 19 zilizonse, zaka 7 zinkakhala ndi mwezi wowonjezera

   

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena