Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 7/12 tsamba 32
  • Zinthu Zidzasinthadi Kodi Inuyo Mudzakhalako?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zinthu Zidzasinthadi Kodi Inuyo Mudzakhalako?
  • Galamukani!—2012
Galamukani!—2012
g 7/12 tsamba 32

Zinthu Zidzasinthadi Kodi Inuyo Mudzakhalako?

● Nkhani zoyambirira m’magazini ino zasonyeza kuti anthu ambiri padziko lonse amafuna zinthu zitasintha. Kodi inuyo mudzakhalako zinthu zikadzasintha padzikoli?

A Mboni za Yehova, omwe amafalitsa magazini ino amakhulupirira kuti Baibulo lingatithandize kudziwa zimene zidzachitike m’tsogolo. Baibulo ndi buku lokhalo limene limafotokoza mbiri ya anthu kuyambira pamene munthu analengedwa. Komanso mosiyana ndi zimene anthu ambiri amakhulupirira, Baibulo limafotokoza kuti m’tsogolomu zinthu zidzakhala bwino.

Buku lakuti Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? lingakuthandizeni kudziwa zambiri zimene Baibulo limafotokoza pa nkhani imeneyi. Bukuli limafalitsidwa ndi Mboni za Yehova ndipo lamasuliridwa m’zinenero 244.

□ Ndikupempha kuti munditumizire bukuli. Lembani chinenero chimene mukufuna.

□ Nditumizireni munthu kuti ayambe kuphunzira nane Baibulo kwaulere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena