Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g16 No. 6 tsamba 16
  • Mlozera Nkhani wa Magazini a Galamukani! a 2016

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mlozera Nkhani wa Magazini a Galamukani! a 2016
  • Galamukani!—2016
  • Timitu
  • ANTHU AKALE
  • CHIPEMBEDZO
  • KUCHEZA NDI ANTHU
  • KUCHITA ZINTHU NDI ANTHU
  • MAYIKO NDI ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • NYAMA NDI ZOMERA
  • SAYANSI
  • UMOYO NDI MANKHWALA
  • ZIMENE BAIBULO LIMANENA
  • ZOSIYANASIYANA
Galamukani!—2016
g16 No. 6 tsamba 16

Mlozera Nkhani wa Magazini a Galamukani! a 2016

“Zikomo kwambiri chifukwa magaziniwa ndi a panthawi yake.”—Amy

Amy ndi mayi yemwe amaona kuti nkhani za m’magazini a Galamukani! ndi zothandiza pa moyo wake watsiku ndi tsiku. Mofanana ndi mayiyu, palinso anthu mamiliyoni ambiri amene magaziniwa amawathandiza kwambiri. Pitani pawebusaiti ya www.jw.org/ny kuti muwerenge nkhani zimene zasonyezedwa m’munsimu.

ANTHU AKALE

  • Aristotle: Na. 5

  • Erasmus, Desiderius: Na. 6

  • Semmelweis, Ignaz: Na. 3

  • Yesu: Na. 5

CHIPEMBEDZO

  • Kodi Baibulo Langokhala Buku Labwino Basi? Na. 2

  • Kodi Baibulo Limalola Kuti Akazi Kapena Amuna Okhaokha Azigonana? Na. 4

  • Kodi Nkhani Yonena za Yesu Ndi Yongopeka? Na. 5

KUCHEZA NDI ANTHU

  • Katswiri Woona za Mmene Ana Osabadwa Amakulira Akufotokoza za Chikhulupiriro Chake (Y. Hsuuw): Na. 2

KUCHITA ZINTHU NDI ANTHU

  • Kodi Mungasonyezane Bwanji Ulemu? (mwamuna ndi mkazi wake): Na. 6

  • Kodi Mungatani Kuti Mukhale ndi Anzanu Apamtima? Na. 1

  • Kuphunzitsa Mwana Wanu Nkhani Zokhudza Kugonana: Na. 5

  • Mungatani Kuti Musamakangane Pokambirana Mavuto Anu? (mwamuna ndi mkazi wake): Na. 3

  • Zimene Mungachite Mwana Akatsala Pang’ono Kutha Msinkhu: Na. 2

MAYIKO NDI ANTHU

  • Kyrgyzstan: Na. 4

  • Liechtenstein: Na. 1

MBONI ZA YEHOVA

  • A Mboni za Yehova Akumasulira M’zinenero Zambiri: Na. 3

  • Kodi Mumadziwa Zotani Zokhudza a Mboni za Yehova? Na. 1

  • “Mfundozi Zindithandiza Kwambiri” (jw.org): Na. 5

NYAMA NDI ZOMERA

  • Mbalame Zokongola Kwambiri: Na. 2

  • Nsomba Yochititsa Chidwi Kwambiri: Na. 6

SAYANSI

  • Chinthu Chodabwitsa (kaboni): Na. 5

  • Kanyama Kam’madzi Komwe Kamasinthasintha Mtundu: Na. 1

  • Khosi la Nyerere: Na. 3

  • Nyenje za Moyo Wautali: Na. 4

  • Ulusi wa Nkhono Yam’madzi: Na. 6

UMOYO NDI MANKHWALA

  • Kodi Kudana ndi Kusagwirizana ndi Zakudya kwa Thupi N’kosiyana Bwanji? Na. 3

  • Kodi Tingapewe Bwanji Matenda? Na. 6

ZIMENE BAIBULO LIMANENA

  • Chikhulupiliro: Na. 3

  • Kukongola: Na. 4

  • Kumwamba: Na. 1

  • Kusunga Nthawi: Na. 6

  • Kuyamikira: Na. 5

  • Nkhawa: Na. 2

ZOSIYANASIYANA

  • Kodi N’zotheka Kusintha Zomwe Munazolowera? Na. 4

  • N’zotheka Kumasangalalabe Ngakhale Muli ndi Mavuto: Na. 1

  • Zimene Mungachite Zinthu Zikasintha: Na. 4

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena