LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • ll masa. 2-3
  • Mau Oyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mau Oyamba
  • Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
ll masa. 2-3

Mau Oyamba

Mulungu ali monga tate wacikondi. 1 Petulo 5:6, 7

Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale Ndi Moyo Wamuyaya

Mulungu ni Mlengi wathu, ndipo amatisamalila. Tate wacikondi amaphunzitsa ana ake. Naye Mulungu amaphunzitsa anthu kulikonse mmene io angakhalile bwino.

Mulungu amatidziŵitsa coonadi camtengo wapatali cimene cimatipatsa cimwemwe ndi ciyembekezo.

Ngati mumamvetsela kwa Mulungu, iye adzakutsogolelani ndi kukuchinjilizani ndipo adzakuthandizani pa mavuto.

Koma palinso zina, mudzakhala ndi moyo wamuyaya!

Mulungu atiuza kuti: ‘Bwelani kwa ine. Mvetselani ndipo mudzakhala ndi moyo.’ Yesaya 55:3

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani