LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mb phunzilo 4
  • Phunzilo 4

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzilo 4
  • Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Mlengi Wathu Wacikondi Amasamala za Ife
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2020
  • Phunzilo 5
    Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Phunzilo 3
    Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
mb phunzilo 4

Phunzilo 4

Machitidwe 14:17

Mailesi adandaula kuti, lelo kuli mvula.

“Siningatuluke panja.

N’cifukwa ciani siileka?”

Tsopano Mailesi wakondwela!

Cifukwa dzuŵa layamba kuwala.

Ndipo mvula yatha.

Ndiyeno athamangila panja, ndipo asangalala, cifukwa paoneka bwino.

Mailesi akamba kuti, “sindinadziŵe kuti ndi Mulungu amene amagwetsa mvula kuti maluŵa amele.”

ZOCITA

Muŵelengeleni mwana wanu:

Machitidwe 14:17

Uzani mwana wanu kuti aloze:

Windo Mbalame Mailesi

Mtengo Maluŵa

Pezani zinthu zobisika.

Kanunda (Cikumbu) Ndege

M’funseni mwana wanu:

N’cifukwa ciani Yehova analenga mvula?

[Cithunzi 10]

[Cithunzi 10]

[Cithunzi 11]

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani