LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w13 9/1 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
w13 9/1 masa. 1-2

Zamkati

September 1, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. All rights reserved.

NKHANI ZOPHUNZILA

OCTOBER 28, 2013–NOVEMBER 3, 2013 | TSAMBA 7 • NYIMBO: 64, 114

Zikumbutso za Yehova Ndi Zodalilika

NOVEMBER 4-10, 2013 | TSAMBA 12 • NYIMBO: 116, 52

Kondwelani Ndi Zikumbutso za Yehova

Yehova nthawi zonse amagwilitsila nchito zikumbutso kuti atsogolele anthu ake. Kodi zikumbutso zimenezi zimaphatikizapo ciani? Nkhani yoyamba ifotokoza zifukwa zimene zingatipangitse kudalila zikumbutso za Mulungu. Yaciŵili idzafotokoza njila zitatu za mmene tingakhalile ndi cidalilo colimba pa zikumbutso za Yehova.

NOVEMBER 11-17, 2013 | TSAMBA 17 • NYIMBO: 69, 106

Kodi Mwasandulika?

NOVEMBER 18-24, 2013 | TSAMBA 22 • NYIMBO: 27, 83

Pangani Zosankha Zanu Mwanzelu

Mmene tinaleledwela ndiponso anthu amene timakhala nao zimatikhudza maganizo athu ndi zosankha zathu. Kodi tingacite ciani kuti zosankha zathu zikhale zogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu? Nanga n’ciani cingatithandize kucita zinthu mogwilizana ndi zosankha zathu? Nkhani zimenezi zidzatithandiza kudzipenda moona mtima pa mbali zimenezi.

NOVEMBER 25, 2013–DECEMBER 1, 2013 | TSAMBA 27 • NYIMBO: 95, 104

Upainiya Umalimbitsa Unansi Wathu ndi Mulungu

M’nkhani iyi tidzakambilana njila 8 zoonetsa mmene upainiya umalimbitsila ubwenzi wa Mkristu ndi Yehova. Ngati ndinu mpainiya, n’ciani cingakuthandizeni kuti mupitilize ngakhale mukumane ndi mavuto? Ngati mufuna kuyamba upainiya ndi kusangalala ndi madalitso ake, kodi mungacite ciani?

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

N’cifukwa Ciani Anthu Akuvutika Kwambili? 3

Mavuto Adzatha Posacedwapa! 5

Kuyankha Mafunso a m’Baibo 32

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani