LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 May masa. 1-2
  • Magazini Yophunzila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Magazini Yophunzila
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 May masa. 1-2
Nsanja ya Mlonda Yophunzila, May 2017

Magazini Yophunzila

MAY 2017

NKHANI ZOPHUNZILA: JULY 3-30, 2017

© 2017 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PIKICA YA PACIKUTO:

ECUADOR

Mpainiya wanthawi zonse alalikila mzimayi wamalonda m’citundu ca Cikwichuwa (Imbabura), pa msika wogulitsila nsalu mumzinda wa Otavalo, kumpoto kwa dziko la Ecuador.

OFALITSA

90,110

MAPHUNZILO A BAIBO

148,637

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2016)

274,593

Magazini ino si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi n’zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo.

Ngati mufuna kupeleka ndalama zothandizila nchitoyi, yendani pa www.jw.org.

Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa ina. Komabe, ena mwa masipeling’i a Cinyanja m’magazini ino tatsatila malamulo a m’buku lakuti A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani