LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 22

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 22
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 22
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 22

MLUNGU WA OCTOBER 22

Nyimbo 71 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 14 ndime 1-5, ndi bokosi pa tsamba 112 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Hoseya 1–7 (Mph. 10)

Na. 1: Hoseya 6:1–7:7 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Gulu la Yehova la Padziko Lapansi Lingadziŵike Bwanji?—rs tsa. 143 ndime 1-7 (Mph. 5)

Na. 3: Tengelani Citsanzo ca Yesu Amene Sanaope Kucititsidwa Manyazi—Aheb. 12:2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 130

Mph. 10: Danga la Mafunso. Kukambilana ndi omvela. Kumbutsani makolo za udindo wao woyang’anila ana ao nthawi zonse popita ndi pobwelako ku Nyumba ya Ufumu, ndi pamene ali pamalo a Nyumba ya Ufumu. Thandizani omvela kudziŵa zinthu zimene zingacititse ngozi pakhomo la Nyumba ya Ufumu, kumalo oikako magalimoto ndi malo ozungulila.

Mph. 10: Samalilani Thanzi Lanu M’njila Yogwilizana ndi Malemba. Kukambilana kozikidwa pa Nsanja ya Olonda ya November 15, 2008, tsamba 25-26, ndime 11-16. Gogomezani kufunika kopewa anthu ocilitsa amene amagwilitsila nchito njila kapena zinthu zokhudzana ndi zamizimu.—gf phunzilo 13 tsa. 21.

Mph. 10: Kodi ‘Mudzamuyesa Yehova’? Nkhani yozikidwa pa Nsanja ya Olonda ya July 15, 2012, masamba 3-6. Gwilitsilani nchito mfundo za mu Nsanjayo pa nkhani yokatumikila kumalo osoŵa m’dela lanu. Ngati alipo, kambilanani ndi wofalitsa mmodzi kapena aŵili amene anakwanitsa kutumikila kumalo osoŵa.

Nyimbo 89 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani