LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 2/13 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 4

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 4
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 4
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 2/13 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa March 4

MLUNGU WA MARCH 4

Nyimbo 62 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 19 ndime 12-20 pa tsa. 152 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Maliko 9–12 (Mph. 10)

Na. 1: Maliko 11:19–12:11 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Munthu Akafa Amalangidwa Cifukwa ca Macimo Ake?—rs tsa. 344 ndime 5-tsa 345 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Munthu Amene Wadzipeleka Kwa Mulungu Amakhala Wacimwemwe?—Mac. 20:35 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 7

Mph. 10: Zimene Mungakambe Pogaŵila Magazini M’mwezi wa March. Kambilanani mafunso otsatilawa:Tikamagawila tumapepala kumapeto kwa mlungu uliwonse, n’ciani cidzatithandiza kuona ngati tingagawilenso magazini? Kodi tidzakamba ciani pogawila magazini tikamaliza kugawila kapepala? Ngakhale kuti zitsanzo za mmene tingagawile kapepala zimaphatikizapo kufunsa funso ndi kuwelenga lemba, kodi tingakagawile bwanji mwacidule? Citani citsanzo ca mmene mungagaŵile magazini iliyonse limodzi ndi kapepala.

Mph. 10: Pindulani ndi kabuku ka Kusanthula Malemba Tsiku ndi Tsiku ka 2013. Nkhani yokambilana. Mwacidule fotokozani lemba la caka limene lili pa masamba 3-4 ndipo muonenso pa tsamba 5 pali mutu wakuti “Mmene Mungagwilitsile Nchito Buku Limeneli.” Ndiyeno funsani omvela kuti afotokoze nthawi imene anakonza kuti azisanthula malemba ndi mmene apindulila. Malizani mwa kulimbikitsa onse kuti azisanthula malemba tsiku lililonse.

Mph. 10: Zosoŵa za Mpingo.

Nyimbo 119 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani