LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 7/13 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 15

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 15
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JULY 15
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 7/13 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa July 15

MLUNGU WA JULY 15

Nyimbo 48 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 26 ndime 1-8, bokosi patsamba 204 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Machitidwe 18–21 (Mph. 10)

Na. 1: Machitidwe 20:17-38 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Anthu Adzaona Kristu Akubwela M’mitambo Kudzatenga Akristu Okhulupilika Kupita Nao Kumwamba?—rs mutu womalizila pa tsa. 213 mpaka tsa. 214 ndime 3 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingasonyeze Bwanji Kuti Timaika Maganizo Athu pa Zinthu za Mzimu?—Aroma 8:6 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 92

Mph. 10: M’fikeni Pamtima Wophunzila Wanu. (Luka 24:32) Nkhani yokambilana yocokela pa mafunso awa: (1) Potsogoza phunzilo la Baibo, n’cifukwa ciani n’kofunika kugogomezela (a) cikondi ca Yehova ndi nzelu zake? (b) kufunika kogwilitsila nchito mfundo za m’Baibo? (c) kufunika kotsatila citsogozo ca Yehova nthawi zonse tisanapange cosankha? (2) Kodi kufunsa phunzilo lanu mafunso otsatilawa kungakuthandizeni bwanji kudziŵa ngati mukum’fika pamtima? (a) Kodi zimenezi zikuoneka kukhala zothandiza kwa inu? (b) Kodi mukuona kuti zimenezi zikugwilizana ndi cikondi ca Mulungu? (c) Kodi mungapeze mapindu otani mukagwilitsila nchito uphungu umenewu?

Mph. 20: “Abale Acinyamata, Kodi Mukukalamila?” Mafunso ndi mayankho. Mwacidule funsani mkulu kapena mtumiki wothandiza amene anakalamila ali wacinyamata. Kodi anapatsidwa nchito ziti komanso anaphunzitsidwa motani asanaikidwe kukhala mtumiki wothandiza? Kodi ena mumpingo anamuthandiza bwanji kupita patsogolo mwa kuuzimu? Kodi apeza madalitso otani kaamba ka kukalamila?

Nyimbo 85 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani