LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 7/13 tsa. 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 29

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 29
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JULY 29
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 7/13 tsa. 7

Ndandanda ya Mlungu wa July 29

MLUNGU WA JULY 29

Nyimbo 51 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 26 ndime 16-22 ndi bokosi patsamba 209 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Macitidwe 26-28 (Mph. 10)

Na. 1: Macitidwe 26:19-32 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Akristu Okhulupilika Adzatengedwa Kupita Kumwamba Mobisa Asanafe?—rs tsa. 215 ndime 2 mpaka tsa. 216 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingadziŵe Bwanji Kuti Mzimu Woyela wa Mulungu Ukugwila Nchito Mwa Atumiki Ake?—Agal. 5:22, 23; Chiv. 22:17 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 96

Mph. 10: Lalikilani Mwacibadwa. NKhani yocokela m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 128, ndime 1, mpaka tsamba 129, ndime 1. Mwacidule funsani wofalitsa waluso amene athetsa manyazi. Kodi n’ciani camuthandiza kuti asazicita manyazi muulaliki?

Mph. 10: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambilana, yokambidwa ndi mkulu.

Mph. 10: Musonyeze Kuti Ndinudi Ana a Atate Wanu Wakumwamba. (Mat. 5:43-45) Nkhani yokambilana yocokela mu Nsanja ya Olonda June 15, 2010, tsamba 25, ndime 1-2 ndi tsamba 27 mpaka 29, ndime 11 mpaka 18. Pemphani omvela kuti anene maphunzilo amene aphunzilapo.

Nyimbo 80 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani