LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/13 tsa. 2
  • “Ndabwela pano kuti . . .”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Ndabwela pano kuti . . .”
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Zofanana
  • Kuongolela Luso Lathu mu Ulaliki—Kukonzekela Mau Athu Oyamba
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kugaŵila Buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 11/13 tsa. 2

“Ndabwela pano kuti . . .”

Eninyumba akatsegula citseko ndi kutipeza taima pakhomo pao, io angafune kudziŵa kuti ndife ndani ndi kuti tabwela kudzatani. Kodi tingadzidziŵikitse bwanji kuti tiŵakhazike mtima pansi? Pambuyo popeleka moni ofalitsa ena amayamba ndi mau akuti “tabwela pano kuti,” ndiyeno amayamba kufotokoza. Mwacitsanzo, anganene kuti: “Tabwela pano kuti ticezeko nanu popeza anthu ambili amadela nkhawa zaupandu. Kodi inu muganiza kuti . . .” Kapena anganene kuti “Ndabwela pano kuti tiziphunzila Baibo kwaulele.” Ngati kuciyambi kwa makambitsilano tamuuza mwininyumba cifukwa cake tam’cezela, angakhale wofunitsitsa kumvetsela zimene tifuna kunena.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani